Sirach 17


Chapters: 1 2 3 4 5 6 7 8 9 10 11 12 13 14 15 16 17 18 19 20 21 22 23 24 25 26 27 28 29 30 31 32 33 34 35 36 37 38 39 40 41 42 43 44 45 46 47 48 49 50 51

Sirach Chapter 17
VerseEnglishCopticDutchFrenchGermanSpanishItalianTurkishSimplified ChineseTraditional ChinesePortugueseIndonesianThaiHindiChichewaUrduArabic
17:1The Lord created human beings out of earth, and makes them return to it again.Der Herr hat die Menschen aus Erde erschaffen und lässt sie wieder zu ihr zurückkehren.Il Signore creò l'uomo dalla terra e ad essa lo fa tornare di nuovo.Mulungu adapanga anthu ndi dothi, ndipo amaŵabwezeranso kudothi komweko.خلق الرب الانسان من الارض
17:2He gave them a fixed number of days, but granted them authority over everything on the earth.Gezählte Tage und eine bestimmte Zeit wies er ihnen zu und gab ihnen Macht über alles auf der Erde.Egli assegnò agli uomini giorni contati e un tempo fissato, diede loro il dominio di quanto è sulla terra.Adaŵalembera masiku oŵerengeka ndi nthaŵi yochepa, koma adaŵapatsa ulamuliro pa zolengedwa zonse.و اليها اعاده
17:3He endowed them with strength like his own, and made them in his own image.Ihm selbst ähnlich hat er sie mit Kraft bekleidet und sie nach seinem Abbild erschaffen.Secondo la sua natura li rivestì di forza, e a sua immagine li formò.Adaŵapatsa mphamvu zonga zake, ndipo adaŵalenga mofanafana naye.جعل لهم وقتا واياما معدودة واتاهم سلطانا على كل ما فيها والبسهم قوة بحسب طبيعتهم وصنعهم على صورته
17:4He put the fear of them in all living beings, and gave them dominion over beasts and birds.Auf alle Wesen legte er die Furcht vor ihnen, über Tiere und Vögel sollten sie herrschen.Egli infuse in ogni essere vivente il timore dell'uomo, perché l'uomo dominasse sulle bestie e sugli uccelli.Zolengedwa zamoyo zonse adazipatsa mantha oopa anthu. Adapatsadi anthu ulamuliro pa nyama ndi mbalame.القى رعبه على كل ذي جسد وسلطه على الوحش والطير
17:5They obtained the use of the five faculties of the Lord; as sixth he distributed to them the gift of mind, and as seventh, reason, the interpreter of one's faculties.[]Discernimento, lingua, occhi, orecchi e cuore diede loro perché ragionassero.Anthuwo adalandira mphamvu zisanu kwa Mulungu, ina yachisanu ndi chimodzi inali ya nzeru za kuganiza bwino, inanso yachisanu ndi chiŵiri inali ya nzeru zolongosolera ntchito za mphamvu zakezo.خلق منه عونا بازائه واعطاهم اختيارا ولسانا وعينين واذنين وقلبا يتفكر
17:6Discretion and tongue and eyes, ears and a mind for thinking he gave them.Er bildete ihnen Mund und Zunge, Auge und Ohr und ein Herz zum Denken gab er ihnen.Li riempì di dottrina e d'intelligenza, e indicò loro anche il bene e il male.Anthuwo adaŵapatsa pakamwa, maso ndi makutu, adaŵapatsanso mtima woganizira.و ملاهم من معرفة الحكمة واراهم الخير والشر
17:7He filled them with knowledge and understanding, and showed them good and evil.Mit kluger Einsicht erfüllte er sie und lehrte sie, Gutes und Böses zu erkennen.Pose lo sguardo nei loro cuori per mostrar loro la grandezza delle sue opere.Adaŵadzaza ndi nzeru zodziŵa zinthu ndi zomvetsa zinthu, ndipo adaŵasonyeza kuti zabwino ndi izi, zoipa ndi izi.و جعل عينه على قلوبهم ليظهر لهم عظائم اعماله
17:8He set his eye upon their hearts to show them the majesty of his works.Er zeigte ihnen die Größe seiner Werke, um die Furcht vor ihm in ihr Herz zu pflanzen.Loderanno il suo santo nome per narrare la grandezza delle sue opere.Mulungu adaikamo kuŵala kwake m'mitima mwao, kuti aŵaonetse ukulu wa ntchito zake.ليحمدوا اسمه القدوس ويخبروا بعظائم اعماله
17:9-Sie sollten für immer seine Wunder rühmenInoltre pose davanti a loro la scienza e diede loro in eredità la legge della vita.Adaŵalola kuti azinyadira ntchito zake zodabwitsa mpaka muyaya.و زادهم العلم واورثهم شريعة الحياة
17:10And they will praise his holy name, to proclaim the grandeur of his works.und seinen heiligen Namen loben.Stabilì con loro un'alleanza eterna e fece loro conoscere i suoi decreti.Choncho iwo adzatamanda dzina lake loyera, adzalalika ukulu wa ntchito zake.و عاهدهم عهد الدهر واراهم احكامه
17:11He bestowed knowledge upon them, and allotted to them the law of life.Er hat ihnen Weisheit geschenkt und ihnen das Leben spendende Gesetz gegeben.I loro occhi contemplarono la grandezza della sua gloria, i loro orecchi sentirono la magnificenza della sua voce.Iye adaŵaninkha nzeru, naŵapatsa Malamulo opatsa moyo.فرات عيونهم عظائم المجد وسمعت اذانهم مجد صوته وقال لهم احترزوا من كل ظلم
17:12He established with them an eternal covenant, and revealed to them his decrees.Einen ewigen Bund hat er mit ihnen geschlossen und ihnen seine Gebote mitgeteilt.Disse loro: «Guardatevi da ogni ingiustizia!» e diede a ciascuno precetti verso il prossimo.Adapangana nawo chipangano chamuyaya, naŵaululira Malamulo ake.و اوصاهم كل واحد في حق القريب
17:13Their eyes saw his glorious majesty, and their ears heard the glory of his voice.Ihre Augen sahen seine machtvolle Herrlichkeit, ihr Ohr vernahm seine gewaltige Stimme.Le loro vie sono sempre davanti a lui, non restano nascoste ai suoi occhi.Motero anthu adaona ulemerero wa Mulungu ndi maso ao, ndipo adamva ulemerero wa mau ake m'makutu mwao.طرقهم امامه في كل حين فهي لا تخفى عن عينيه
17:14He said to them, Beware of all evil. And he gave commandment to each of them concerning the neighbor.Er sprach zu ihnen: Hütet euch vor allem Unrecht! Er schrieb ihnen ihr Verhalten gegenüber dem Nächsten vor.Su ogni popolo mise un capo, ma Israele è la porzione del Signore.Iye adaŵauza kuti, “Lewani choipa chilichonse,” ndipo adaphunzitsa munthu aliyense m'mene azikhalira ndi anzake. Za kuweruza kwa Mulunguلكل امة اقام رئيسا
17:15Their ways are always known to him; they will not be hid from his eyes.Ihre Wege liegen allezeit offen vor ihm, sie sind nicht verborgen vor seinen Augen.Tutte le loro opere sono davanti a lui come il sole, i suoi occhi osservano sempre la loro condotta.Machitidwe a anthu amadziŵika pamaso pa Mulungu nthaŵi zonse, sangathe kubisika konse pamaso pake.اما اسرائيل فهو نصيب الرب
17:16-[]A lui non sono nascoste le loro ingiustizie, tutti i loro peccati sono davanti al Signore.Kuyambira ali ana, machitidwe ao adapendekera ku zoipa, akulephera kusandutsa mitima yao youma ngati miyala kuti ikhale yofeŵa ngati mnofu.جميع اعمالهم كالشمس امامه وعيناه على الدوام تنظران الى طرقهم
17:17He appointed a ruler for every nation, but Israel is the Lord's own portion.Für jedes Volk bestellte er einen Herrscher, Israel aber ist der Erbbesitz des Herrn.La beneficenza dell'uomo è per lui come un sigillo, egli serberà la generosità come la propria pupilla.Mtundu uliwonse adaupatsa mtsogoleri wake, koma adasankha Aisraele kuti akhale choloŵa chake.لم تخف عنه اثامهم بل جميع خطاياهم امام الرب
17:18-[]Alla fine si leverà e renderà loro la ricompensa, riverserà su di loro il contraccambio.Amaŵaphunzitsa mwambo poti ndi ana ake achisamba, amaŵaunikira ndi chikondi chake ndipo saŵasiya.صدقة الرجل كخاتم عنده فيحفظ احسان الانسان كحدقة عينه
17:19All their works are as clear as the sun before him, and his eyes are ever upon their ways.Alle ihre Taten stehen vor ihm wie die Sonne, seine Augen ruhen stets auf ihren Wegen.Ma a chi si pente egli offre il ritorno, consola quanti vengono meno nella pazienza.Ntchito zao zonse zili ngati dzuŵa pamaso pake, amaziyang'anitsa nthaŵi zonse.و بعد ذلك يقوم ويجازيهم يجازيهم جزاءهم على رؤوسهم ويهبطهم الى بطون الارض
17:20Their iniquities are not hidden from him, and all their sins are before the Lord.Ihre Frevel sind vor ihm nicht verborgen, alle ihre Sünden stehen dem Herrn vor Augen.Ritorna al Signore e cessa di peccare, prega davanti a lui e cessa di offendere.Zoipa zao sizibisika pamaso pa Ambuye, Iwo amaona machimo ao onse.لكنه جعل للتائبين مرجعا وعزى ضعفاء الصبر ورسم لهم نصيب الحق
17:21-[]Fà ritorno all'Altissimo e volta le spalle all'ingiustizia; detesta interamente l'iniquità.Ambuye ngokoma mtima, amadziŵa zolengedwa zao, saziwononga kapena kuzisiya, koma amazisunga.فتب الى الرب واقلع عن الخطايا
17:22One's almsgiving is like a signet ring with the Lord, and he will keep a person's kindness like the apple of his eye.Das Almosen eines jeden ist bei ihm wie ein Siegelring, des Menschen Wohltat behütet er wie einen Augapfel.Negli inferi infatti chi loderà l'Altissimo, al posto dei viventi e di quanti gli rendono lode?Munthu akathandiza osauka, kwa Ambuye chithandizocho chili ngati mphete yamtengowapatali, ndipo chifundo chimenecho kwa Ambuye chili ngati mwana wa diso lao.تضرع امام وجهه واقلل من العثرات
17:23Afterward he will rise up and repay them, and he will bring their recompense on their heads.Schließlich erhebt er sich und vergilt ihnen, er lässt die Vergeltung über ihr Haupt kommen.Da un morto, che non è più, la riconoscenza si perde, chi è vivo e sano loda il Signore.Potsiriza pake adzadzambatuka nadzalipira onse, ndipo adzaŵabwezera zonse pamutu pao monga kuyenera.ارجع الى العلي واعرض عن الاثم وابغض الرجس اشد بغض فهل من حامد للعلي في الجحيم
17:24Yet to those who repent he grants a return, and he encourages those who are losing hope.Den Reumütigen aber gewährt er Umkehr und tröstet die Hoffnungslosen [und bestimmte sie für ein Leben in der Wahrheit].Quanto è grande la misericordia del Signore, il suo perdono per quanti si convertono a lui!Komabe munthu wolapa Ambuye amampatsa mpata kuti abwerere kwa Iwo, ndipo munthu wa khama lofookerapo Ambuye amamlimbitsa mtima. Aŵauza kuti atembenuke mtimaتعلم اوامر الله واحكامه وكن ثابتا على حظ التقدمة والصلاة للعلي
17:25Turn back to the Lord and forsake your sins; pray in his presence and lessen your offense.Wende dich zum Herrn, lass ab von der Sünde, bete vor ihm und beseitige das Ärgernis!L'uomo non può avere tutto, poiché un figlio dell'uomo non è immortale.Tsono bwerera kwa Ambuye, ndipo leka zoipa zako. Upemphere kwa Ambuye, ndipo uchepetse machimo ako.ادخل في ميراث الدهر المقدس مع الاحياء المعترفين للرب
17:26Return to the Most High and turn away from iniquity, and hate intensely what he abhors.Kehre zum Höchsten zurück und wende dich ab vom Bösen, hasse stets das Schlechte!Che c'è di più luminoso del sole? Anch'esso scompare. Così carne e sangue pensano al male.Bwerera kwa Mulungu Wopambanazonse, ndipo lekeratu kuchimwa. Udane nazo kwambiri zonyansa zonse.لا تلبث في ضلال المنافقين اعترف قبل الموت فان الاعتراف يعدم من الميت اذ يعود كلا شيء
17:27Who will sing praises to the Most High in Hades in place of the living who give thanks?Wer wird in der Unterwelt den Höchsten loben anstelle derer, die leben und ihn preisen?Esso sorveglia le schiere dell'alto cielo, ma gli uomini sono tutti terra e cenere.Tingatamande bwanji Mulungu Wopambanazonse pamene tili m'manda, ngati sitimtsira ulemu pamene tili moyo?انك ما دمت حيا معافى تحمد الرب وتفتخر بمراحمه
17:28From the dead, as from one who does not exist, thanksgiving has ceased; those who are alive and well sing the Lord's praises.Beim Toten, der nicht mehr ist, verstummt der Lobgesang; nur der Lebende und Gesunde preist den Herrn.Anthu akufa sangathe kutamanda, ali ngati anthu amene kunalibe chikhalire. Okhaokhawo amene ali ndi moyo angathe kutamanda Mulungu.ما اعظم رحمة الرب وعفوه للذين يتوبون اليه
17:29How great is the mercy of the Lord, and his forgiveness for those who return to him!Wie groß ist das Erbarmen des Herrn und seine Nachsicht gegen alle, die umkehren zu ihm.Ndithu chifundo cha Ambuye nchachikulu, ndipo amakhululukira onse obwerera kwa Iwo.لا يستطيع الناس ان يحوزوا كل شيء لان ابن الانسان ليس بخالد
17:30For not everything is within human capability, since human beings are not immortal.Denn nicht wie Gott ist der Mensch, Gottes Gedanken sind nicht wie die Gedanken der Menschen.Munthu sangathe kukhala ndi zonse, poti ana a anthu sadzakhalapo mpaka muyaya.اي شيء اضوا من الشمس وهذه ايضا تكسف والشرير يفكر في اللحم والدم
17:31What is brighter than the sun? Yet it can be eclipsed. So flesh and blood devise evil.Was ist heller als die Sonne? Und selbst sie verfinstert sich; so ist auch das Begehren von Fleisch und Blut böse.Kodi chilipo china choŵala kupambana dzuŵa? Komabe mwina kuŵala kwa dzuŵa kumaleka. Momwemonso munthu wamnofu ndi wamagazi sakhalira kuganiza zoipa.الرب يستعرض جنود السماء العليا اما البشر فجميعهم تراب ورماد
17:32He marshals the host of the height of heaven; but all human beings are dust and ashes.Das Heer in der Höhe zieht er zur Rechenschaft, erst recht die Menschen, die nur Staub und Asche sind.Mulungu amayang'anira nyenyezi zamumlengalenga, koma anthu onse ndi fumbi ndi phulusa chabe.